Category Archives: Uncategorized

23-0226 Fyuluta Ya Munthu Woganiza

Uthenga: 65-0822M Fyuluta Ya Munthu Woganiza

PDF

BranhamTabernacle.org

Okondedwa Osonkhana Ndi M’bale Branham,

Ndikufuna kuitana dziko kuti lisakane naife pa kulumikizanitsa Lamlungu lino pa 12:00 P.M., nthawi ya Jeffersonville, pamene ife a chiomba nkanga timasonkhana pamodzi mailosi mazana awiri aliwonse mu umodzi wa mipingo ya mneneri. Tidzamva Mulungu akulankhula kupitira mu mngelo mutumwa Wake wachisanu ndi chiwiri ndi kutiuza kuti:

Uthenga uwu, ndi Mauthenga ena onse amene ine ndimalankhula, walunjikidwa kwa osonkhana anga. Izo si za osonkhana anu koma ngati iwo akufuna kuti achilandire Icho. Koma Izo zalunjikidwa kwa anthu awa pano.

Iye akulankhula kwa ife, ULEMERERO, osonkhana ake. Osati inu amene mumati, “M’bale Branham ndi mneneri, koma iye si m’busa wanga. Abusa athu akuti kuliza matepi mu tchalitchi simolingana ndi Mawu amasiku ano.” “M’busa wathu amatiuza kuti tizimumvera. Molingana ndi Mawu, akutitsogolera ndi Mzimu Woyera tsopano.”

Mneneri anakulankhulani inu ndi abusa anu.

Kwa atumiki aliwonse pa malo aliwonse, nthawi iliyonse, izi sizinalunjikidwe monyozera ku ziphunzitso zanu, izi sizinalunjikidwe nkomwe kwa nkhosa zanu.

Sitifuna kukangana nanu abale ndi alongo. Ife tikumvetsa, Izo sizinalunjikidwe kwa inu, koma kwa ife, amene timakhulupirira kuti Mzimu Woyera wayika mngelo Wake wachisanu ndi chiwiri mutumiki kuti akhale m’busa wathu ndi kutitsogolera ife, mpingo Wake. Ife timakhulupirira kuti kuliza matepi ndi NJIRA YAZOONA YOKHA. Mulichabebwino ndipo mukuchita zomwe mneneri wakuuzani kuti muchite:

Ndipo ine nthawizonse ndimalozera kwa iwo, ngati iwo ali membala wa mpingo wina, “Kawoneni abusa anu.”

Muyenera kuchita monga momwe abusa anu akunenera.

Kenako mneneri amauza abusa anu, kuti atsimikize kuti amvetsetse.

Tsopano, abusa, ine ndikufuna inu mudziwe izo, kuti, izi ndi kwa osonkhana anga okha omwe ine ndimalankhula zinthu izi. Ndipo ine ndiri nawo ufulo wochita zimenezo, chifukwa ine ndinaikidwa ndi Mzimu Woyera kuti ndiziyang’anira nkhosa izi.

Watumidwa kuti aziyang’anira ife, nkhosa zake; amene Mulungu wawaika mu zisamaliro AKE. Mzimu Woyera ndi m’busa wathu pamene Iye akulankhula kwa ife ndi kutitsogolera ife tsiku lirilonse ndi Liwu Lake lotsimikiziridwa.

Izi ndi zimene Yehova akutitsogolera kuchita. Ife sitikutsutsa inu kapena abusa anu, kapena momwe inu mukumverera kutsogozedwa ndi Ambuye kuti muchite. Munthu aliyense ayenera kuchita zimene akuona kuti Yehova akumutsogolera kuchita mogwirizana ndi Mawu.

Tili ndi chosefela chimodzi, UTHENGA UWU. Chirichonse chimene timamva chiyenera kupita mu sefa imeneyo. Liwu limene timamva pa matepi ndilo Liwu lokha lomwe tili nalo 100% kukutila kuti NDI KULANKULA KWA AMBUYE.

Kodi inu mukhulupirira kuti kudzoza kumeneko pa anthu amenewo kutanthauza kuti ndi kudzoza kwa Mzimu Woyera?” Inde, bwana, Mzimu Woyera weniweni wa Mulungu pa munthu, koma iwo ndi abodza.

Kopita kwathu Kwamuyaya zimatengera zomwe IYE ANENA PATEPI, osati zomwe munthu wina aliyense kapena gulu la anthu likunena. Choncho, sitingathe, ndipo sitidzamva wina aliyense. Kodi munthu angachite bwanji mwayi?

Bwerani mudzasonkhane pamodzi ndi ife mochulukira, popeza muona kuti tsiku lilikuyandikira.

Anthu akhoza kukhala mnyumba zawo momwemo kapena mwawo…kusonkhana m’malo awo, matchalitchi awo, ndi zina zotero, ndi kumvetsera misonkhano.

Kuti, abwenzi anga, molingana ndi mneneri wa Mulungu, osati kutanthauzira kwa munthu wina pa zomwe Baibulo limanena, tikudzisonkhanitsa tokha pamodzi mozungulira Mawu mochuluka kwambiri momwe ife tikuwonera tsiku likuyandikira.

Kodi chingalawa popanda Mulungu n’chabwino bwanji? Ndi bokosi yankuni chabe, magome angapo amiyala.

Bwerani mudzasonkhane nafe pamene tikumvera chosefela choperekedwa ndi Mulungu, pamene akutibweretsera Uthenga: Chosefela Cha Munthu Woganiza 65-0822E.

M’bale. Joseph Branham

Onani zomwe mukumenyera. Onani zomwe mulili pano. Yang’anani zomwe mumapitira kutchalitchi. Zomwe zimakupangitsani inu…Ndi zabwino kupita ku tchalitchi, koma osanpita ku tchalitchi kokha; izo sizingakupulumutseni inu.

23-0219 Khristu Akuwululidwa Mu Mawu Ake Omwe

Uthenga: 65-0822M Khristu Akuwululidwa Mu Mawu Ake Omwe

PDF

BranhamTabernacle.org

Nkhosa zanga zazing’ono,

Moni kwa inu ndi inu pama foni awa, zabwino kwambiri.Ndine wothokoza kwambiri kwa Ambuye inu mukhoza kukhala mnyumba mwanu momwe, kusonkhana mu malo anu, mipingo yanu, ndi kumva bulaliki. Kulikonse kumene liwu langa likubwera, lekani gulu laling’ono ilo lidalitsidwe.

Lero, ndikufuna kukulemberani kalata yachikondi yochokera pansi pamtima kuti ndikulimbikitseni. Inu ndinu amene Mulungu anasankha kuti mukhale Mkwati Wake kuchokela kuchiyambi cha dziko; inu mukumvera matepi aya. Ine ndikuuzani inu nthawi zambiri, matepi aya ndi anu okha, ndinu osonkhana anga. Ine ndiribe udindo pa zomwe Mulungu anapatsa atumiki ena kuti azidyese; Ndili ndi udindo pa mtundu wa Chakudya chomwe ndimakupatsirani. Matepi aya ndi a inu, mpingo wanga yekha, amene Mulungu wandipatsa kukala mbusa. Ndi Manna obisika, winayo sangakhoze kutenga Izo.

Tsopano, ngati anthu ena akufuna kupanga haibridi chakudya ndi zinthu kunja uko, asiyeni iwo atenge vumbulutso kuchokera kwa Mulungu ndi kuchita zomwe Mulungu akuwauza iwo kuti azichita, azidya pa chirichonse chimene iwo akufuna. Ndichita zomwezo. Koma Mauthenga awa nkwa inu nokha.

Ine ndikuyesera mwakukhoza kwanga kukhala ndi Mawu, kwa inu amene mwayikidwa mmanja mwanga kuchokera kwa Mulungu, chifukwa nkhosa zimafuna chakudya cha nkhosa. “Nkhosa Zanga zimamva Liwu Langa.” Ndipo ndicho chimene ife timakhalira moyo, Mawu aliwonse amene atuluka. Osati Mawu chabe nthawi ndi nthawi, koma Mawu aliwonse amene atuluka kuchokera mkamwa mwa Mulungu. Ndi chimene inu oyera mtima mumakhala nayho.

Aliyense ayenera kukhala ndi chinachake chimene angagwire .Chinachake chiyenera kukhala chomangirira, mwa kuyankhula kwina, chodalirapo. Ndipo aliyense ayenera kukhala nacho mtheradi kapena mtheradi. Kwa ine, ndi kwa iwo amene ine ndikuyembekeza kuti ine ndikuwatsogolera kwa Khristu, ndi mwa Khristu, Baibulo ndilo chochidalira chathu.

Tsopano, ife tikuzindikira kuti Mulungu anatitumizira ife aneneri Ake. Umo ndi momwe Iye aliri ndi kubweretsa Mawu Ake kwa anthu, kupitila mu milomo ya mneneri Wake. Tsopano mu masiku otsiriza ano, Iye walonjeza kuti adzadziwonetsera Yekha mu chidzalo kachiwiri, cha thupi Lake, mu Mzimu. Ndi Mulungu Mwiniwake mu mawonekedwe a chilembo, mawonekedwe a mneneri, akuwonetseredwa mu thupi.

Ine ndiyenera kukhala lyonse mu Kukhalapo kwa analemba ndi cholembera changa chokonzeka nthawi iliyonse kuti nilembe chirichonse chimene Iye anena. Ine ndimayika maganizo anga pa maganizo Ake; osati zomwe munthu amaganiza, zomwe m’badwo ukuganiza, zomwe mpingo ukuganiza, zomwe ufumu ukuganiza. Maganizo a Mulungu okha! Ndimangofotokoza maganizo a Mulungu ku Mawu.

Pamene Mulungu awulula maganizo Ake kwa ine, ine ndimazifotokoza izo mu Mawu kwa inu pa tepi, “KUKAMBA KWA AMBUYE.” Izo siziri, “Kukamba kwa ine.” Ndi, “KUKAMBA KWA AMBUYE!” Ine ndingakhoze kokha kuwatanthauzira Iwo monga Analemba anivomeleza ine kuti ndikutanthauzire kwa inu; pakuti Iwo ali Mawu osalephera a Mulungu.

Alipo ena ambiri amene amayesa kunikopela ine, monga ansembe, ndi zina zotero. Ndipo amachita chiyani? Ingosokonezani, ndizo zonse. Iwo sakhoza kuchita izo. Mulungu anandituma ine, mneneri Wake, kuti ndidzamutsogolere Mkwati Wake; osati munthu wina, kapena osati gulu la amuna.

Mawu omwe ndikunena, ndi momwe ndimachitira, adzachititsa khusaona ena, koma adzatsegula maso a ena. Iye anandivalika ine mu mtundu wa diresi limene ine ndifunika ndivale, chikhalidwe changa, chikhumbo changa, chirichonse basi momwe ine ndiyenera kukhalira. Anakusankhirani ine mwabwino. Ena amaima ndi kuyang’ana ndi kunena, “Chabwino, sindingathe. Pali…ine—ine sindikukhoza kuwona.” Iwo achititsidwa khusaona.

Adzaulula kwa amene Iye adzaulula. Iye anapangidwa kotero kuti Iye akhoza kudzibisa Yekha mu Lemba, kwa wazamulungu wochenjera kwambiri amene alipo. Iye akhoza kungodzibisa Yekha, kukhala apo pomwe mu Lemba, ndipo iwo akhoza kuyang’ana utali wa tsiku lonse ndipo osachiwona icho; kuyang’anani moyo wonse, ndipo osachiwona icho. Iye akhoza kungodzibisa Yekha, kunkhala pamenepo.

Chofunikira tsopano ndi iwo amene alandira Uthenga mu mitima yawo, ayenera kunkala mu Kukhalapo kwa Mwana, kuti akachepe. Lisani matepi ndiyeno lolani Mwana aphike zobiriwira zonse mwa inu, kukupangani inu Akhristu okhwana.

Pamene iye anabwera nthawi yoyamba, iye anali munthu. Pamene iye anabwera nthawi yachiwiri; ndi magawo awiri, iye anali munthu. Pamene iye anabwera mu mawonekedwe a Yohane M’batizi, iye anali munthu. Iye analonjeza kubwera tsiku lino ndi kukhala moyo ndi kudziulula Yekha kamodzinso mwa munthu; Mwana wa munthu akukhala m’thupi la munthu.

Ife tsopano tiri mu m’badwo wa Maso, aulosi, wa Malaki 4. Palibe china chatsalira kuti icho chibwere koma Iye Mwiniwake kuti alowe mu zimenezo, ’chifukwa ndicho chinthu chotsiriza chimene chiripo.

Mvetserani ana ankhosa anga, inu amene Mulungu wandipatsa ine kwa m’busa. Nthawi lachedwa. Iye azabwela posachedwa, Mkwati Wake. Khalani nawo matepi amenewo, ayo siyafunika kutanthauzira.

Ine ndikukuitanani inu a Mphungu aang’ono kuti mubwere mudzalumikizana nane ndi chinthu chokha chimene chidzabweretse Mkwati Wake pamodzi Lamlungu lino, pa 12:00 p.M., nthawi ya Jeffersonville. Mudzamva Kukamba kwa Ambuye pamene Mulungu akulankhula kupyolera mwa ine ndi kuwulula: Khristu Akuwululidwa Mmawu Ake 65-0822M.

Kumbukirani, KHALANI NDI UTUMIKI WA TEPI.LISANI MATEPI TSIKU LONSE.

M’bale Branham

Malemba o werenga pamene mukalibe kumva Uthenga:

Eksodo 4:10-12
Yesaya 53:1-5
Yeremiya 1:4-9
Malaki 4:5
Luka 17:30 St
Yohane Woyera 1:1 / 1:14 / 7:1-3 / 14:12 / 15:24 / 16:13
Agalatiya 1:8
2 Timoteyo 3:16-17
Ahebri 1:1-3 / 4:12 / 13:8
2 Petulo 1:20-21
Chivumbulutso 1:1-3 / 10:1-7 / 22:18-19

23-0212 Ndipo Osadziwa Izo Ayi

Uthenga: 65-0815 Ndipo Osadziwa Izo Ayi

PDF

BranhamTabernacle.org

Wokondedwa Mkwati Akuyembekezera,

Ndipo ine ndikudziwa kuti, ndizakachoka pa dziko lapansi lino, matepi awo ndi mabuku amenewo adzakhala ali moyo, ndipo ambiri a inu ana aang’ono mudzapeza, mu masiku akubwela, kuti izi ziri ndendende Choonadi, chifukwa ine nachiyankhula icho mu. Dzina la Ambuye.

Bwerani mudzasonkhane nafe a Eagles, Lamlungu nthawi ya 12:00 PM. Jeffersonville nthawi, pomwe ife tikumva 65-0815, Ndipo Osadziwa Izo Ayi

Bro. Joseph Branham

23-0205 Zochitika Zimamveka Bwino Ndi Uneneri

Uthenga: 65-0801E Zochitika Zimamveka Bwino Ndi Uneneri

PDF

BranhamTabernacle.org

Okondedwa Anthu a nthawi,

Atate, timakukondani kwambiri. Kodi tingayambe bwanji kufotokoza maganizo athu? Inu munatisankha ife, munatikonzeratu ife, ndi kukhala Munthu wamoyo kuti mupereke Moyo Wanu kwa ife.

Inu munalemba maganizo Anu omwe kwa ife mwa aneneri Anu, kotero ife tikhoze kukhala nawo Mawu Anu. Ndiye, monga Inu munalonjeza, Inu munabwela kamodzinso, kudziwulula Nokha mu thupi la munthu ndi zochitika zowonetseredwa bwino ndi uneneri, kuti muzitanthauzira ndi kuwulula Mawu Anu.

Mwa kusankha Kwanu komwe, Inu munasankha William Marrion Branham kuti akhale mwamuna wa nthawi. Munamusankha kuti skate kuganiza kwathu. Inu munayendesa manja ake. Munayendesa maso ake m’masomphenya. Iye sakanakhoza kunena kanthu koma zomwe Inu munamuwonetsa iye.

Iye sakanakhoza kuyankhula kanthu koma chimene Inu munachiika mkamwa mwake. Munali ndi mphamvu zonse za lilime lake, zala zake, ndi chiwalo chilichonse cha thupi lake. Iye anali mu ulamuliro wathunthu ndi Inu.

Ndiye, mwa kusankha Kwanu kamodzinso, Inu munatisankha ife kuti tikhale anthu a nthawi ino. Gulu lanu laling’ono losonkhanitsidwa ndi kudzoza kwa Mawu Anu, kupanganso, Moyo wa Yesu Khristu. Ndife Mawu Anu kujowina Mawu. Palibenso china chimene tingachite.

Atate, tikufuna kukhala mu chifuniro Chanu chabwino; palibe china chofunika kwa ife. Ife sitikufuna maganizo athu, maganizo athu, kapena zomwe munthu wina aliyense anena, chifuniro Chanu chokha.

Ife tapita ku Mawu Anu kuti tiwone chimene Inu munati ife tiyenera kuchita kuti tikhale Mkwati Wanu. Inu munati Inu mudzaweruza dziko tsiku lina mwa Mawu Anu. Inu munatiuza ife kuti Mawu Anu OKHA abwela kwa aneneri Anu OKHA, amene anakonzedweratu ndi kukonzedweratu ndi Inu.

Inu munatiuza ife kuti Izo sizimabwela konse kwa wazamulungu kapena gulu la anthu, koma mwa mneneri Wanu. Iye adzakhala Inu ndinu wotanthauzira Wauzimu yekha wa Mawu. Si maganizo ake, malingaliro ake, kutanthauzira kwake, koma Inu mukuyankhula kupyolera mwa iye, kutanthauzira Mawu Anu Omwe.

Mu m’badwo uliwonse, anthu amalola anthu kuika kutanthauzira kwawo kwawo ku Mawu Anu, ndipo izo zimawapangitsa iwo kuti achititsidwe kusaona. Ilo likuchita chinthu chomwecho chimene chinachita ndi Afarisi ndi Asaduki. Ndicho chifukwa chake anthu amalephera kuti awatenge Iwo lero. Iwo akumvetsera ku zomwe winawake akunena za Iwo, mmalo moti azimvetsera ku Mawu monga mneneri Wanu anawauzira iwo kuti azichita.

Inu munati, choyamba Ine nditumiza Mawu Anga, ndiye ngati anthu sadzakhulupirira Mawu Anga, ndiye Ine ndikuwatumizira iwo utumiki. Munatinso mu m’badwo uliwonse utumiki umasokera; osati onse, koma ambiri a iwo, ndikuwatsogolera anthu kwa iwo okha. Tikufuna kukhala mu Pulogalamu Yanu yoyambirira.

Ndizosokoneza kwambiri, atumiki sangagwirizane pakati pawo. Mbale. X sangagwirizane ndi make. Y; mbale. Y Sindimagwirizana ndi mbale. Z. Sangagwirizane wina ndi mzake. Amangowoneka akugwirizana pa chinthu chimodzi, tisalize matepi mu mpingo.
Ndi Babuloni kachiwirinso, kosokoneza kwambiri. Ife timakhulupirira kuti pali Chitsanzo chimodzi chokha ndipo ife tiyenera kudzicheka tokha kuti tigwirizane ndi Chitsanzo chimenecho, osati kuyesa kudula Chitsanzocho kuti chitikwanira ife.

Pakhala pali mautumiki ochuluka omwe adzuka ndi maganizo awo awo, kutanthauzira kwawo kwawo ndi ziphunzitso. Onse apita pachabe. Pakhala pali atumiki odzozedwa aakulu akuwuka amene amati iwo akulalikira ndi kubwereza Uthenga wa onthawi, ndipo utumiki wawo ndi Njira yoperekedwa ndi Mulungu ya lero, osati matepi.

Iwo ali ndi anthu okhulupirika amene amapita ku mipingo yawo, kuwamvetsera kwa zaka zambiri. Iwo ali ndi azitumiki ambiri ochezera, misonkhano, zitsitsimutso, kulalikira, kunena zomwe iwo amati ndi Njira Yanu yoperekedwa, osati matepi. Ndiye tsiku lina iwo amati, Uthengawo si yachengi.

Kodi iwo sanali kufufuza zimene iye anali kunena ndi matepi? Kodi iwo ankangotenga chimene iye ananena kukhala Mawu, Njira yoperekedwa ndi Mulungu ya lerolino? Ngati iye akanati aziliza matepi, Liwu Lanu lotsimikiziridwa kwa anthu, mmalo mwake kudziyika okha ngati liwu lofunika kwambiri, iwo akanadziwa chimene iwo anali kumva kuti anali wodzozedwa wabodza akuphunzitsa mu nthawi yotsiriza.

Izi sizikutanthauza kuti simukusowa m’busa. Izi sizikutanthauza kuti onse ndi azibusa odzozedwa abodza. Izi sizikutanthauza kuti alipo ambiri amene akulalikira ndendende zomwe M’bale Branham ananena. Izo zikutanthauza chinthu chofunika kwambiri chimene inu muyenera kumva ndi Uthenga wa pa matepi; Ndi KUKAMBA KWA AMBUYE YEKHA.

Ndilo Chitsogozo. Iwo ndiwo Mtheradi. Iwo ali Mawu otsiriza. Iwo ali Mawu Abwino okha. Pokhapokha m’busa, mtsogoleri wanu wauzimu, akumvetsera kwa Mawu abwino awo ndi anthu ake, chinachake chidzalakwika.

Chifukwa chiyani utumiki sakuliza Liwu Lanu lotsimikiziridwa mu mipingo yawo? Iwo anganene bwanji kuti izo ndi zolakwika pamene iwo amadzinenera kuti iwo amakhulupirira kuti Iwo ndi Mawu? Nchifukwa chiyani iwo akupanga zowiringula zamitundu yonse ndi kuti utumiki wawo ndi Njira Yanu yoperekedwa ya lero, osati Liwu Lanu lotsimikiziridwa pa tepi?

Chifukwa chiyani amawopseza anthu ponena chifukwa timati “TYANKANI KULIZA” kuti timve Liwu Lanu, tikupembedza munthu osati Inu kuyankhula kupitila mwa munthu ameneyo?

Timapempela INU EKHA ATATE. Timazifufuza ndi Mawu Anu mobwerezabwereza. Inu mutiuze ife kupyolera mwa mneneri Wanu ndi Uthenga uliwonse umene ife timaumva pa matepi: Ndiye Njira Yanu yokha yoperekedwa ya lero.

Ndi kuti kwina komwe Mkwati Wanu angakhoze kupitako koma kulondolera ku Mawu Anu. Ndife Namwali Wanu Mawu Mkwati. Ife tiyenera kukhala ndi Lawi Lanu la Moto. Ndi malo okhawo omwe tingakhutitsidwe ndikunena kuti ameni ku Mawu aliwonse omwe timawamva.

Atate, ife tikukuwonani Inu kunja kwa mpingo Wanu mukuyesera kulowa mkati, ndipo izo zimaswa mtima wathu. Chotchinga chili mkati ndipo tatsegula chitseko kuti Inu mulowemo. Sitikudziwa china chilichonse. Sitikufuna china chilichonse. Sitingathe kutenga china chilichonse. Ife tapatsidwa pakati ndi Mawu Anu.

Zikomo Atate chifukwa cha Vumbulutso la Mawu Anu. Ife sitikutsutsana ndi aliyense, ife tiri chabe chifukwa cha Mawu anu omveka bwino mwa uneneri. Ife tidzayima pamaso Panu tsiku lina mu chiweruzo. Ndi mitima yathu yonse tikufuna kunena kuti, “Atate, takhala ndi Mawu Anu.”

Limbikitsani abusa anu, mtsogoleri wanu wauzimu, kuti asityanka kuliza Lamlungu lino ndikumva Liwu la Mulungu. Inu mudzaweruzidwa tsiku lina ndi zomwe Mawu a Mulungu amanena pa matepi. Kodi mungapeze bwanji mwayi ndi china chilichonse?

Mwayitanidwa kuti mubwere kudzabwera nafe Lamlungu lino nthawi ya 12:00 PM, nthawi ya Jeffersonville, kuti mudzamve:Events made clear By prophecy 65-0801e, ponders mulungu akhulankula kupitila pamilomo yamuntu omwe anasanka. Mmodzi omwe Iye anapereka kwa gulu lake, mphatso yake. Anamupatsa chikhalidwe chake, makhalidwe ake, ndi chirichonse chimene chingakhale, mmene amadzinenera, ndi chirichonse chimene amachita. Iye anamupanga William Marrion Branham munthu wa nthawi kuti agwire anthu a nthawi, ndipo ife ndife ANTHU A NTHAWI .

Mbale. Joseph Branham

Malemba:
Genesis: 22:17-18
Masalimo: 16:10 / chaputala 22 / 35:11 / 41:9
Zekariya 11:12; 13:7
Yesaya: 9:6/40:3-5/50:6/53:7-12
Malaki: 3:1/4 mutu
Yohane 15:26
Luka Woyera: 17:30 / 24:12-35
Aroma 8:5-13
Ahebri: 1:1/13:8
Chivumbulutso: 1:1-3 / Chaputala 10

23-0129 Mulungu Wa M’badwo Woipa Uno

Uthenga: 65-0801M Mulungu Wa M’badwo Woipa Uno

PDF

BranhamTabernacle.org

Wokondedwa Namwali wamung’ono wa Khristu, Mawu, Nkhosa,

Sitingakhale chinanso. Sitingamve china chilichonse. Sitikudziwa china chilichonse. Sitikufuna china chilichonse. Kumene kuli Nyama yatsopano, KUTYAKA KULIZA, amene ali Mawu a nyengo, kumeneko mphungu zidzasonkhana. Mawu obwera kumoyo mwa ife.

Sitili ndi wina aliyense! Inu ndinu anthu opatulidwa, oyera kwa Ambuye, odzipereka kwa Mawu ndi Mzimu wa Mulungu, kuti mubale chipatso cha lonjezo Lake la tsiku lino. Timakula nthawi zonse ndi kukhwima pomva Mau a Mulungu.

Mneneri anatiuza ife kuti tiloze mmbuyo ku matepi awa. Ngati muli ndi makina a tepi, sonkhanitsani gulu la anthu ndi kutyaka iyo, ndipo mvetserani mwatchifupi. Mvetserani ku Liwu Lake, zomwe Iye akutiuza ife. Mawu a Mulungu safuna kutanthauzira; Iye amachita kutanthauzira Kwake Kwake. “Ine ndine Liwu la Mulungu kwa inu.”

Ndipo ili ndi Ilo, Baibulo, palibe mawu amodzi oti awonjezedwe kwa Ilo kapena kuchotsedwa kwa Ilo. Ingokhalani kumene ndi Liwu limenelo. “Mlendo sangamutsatire,”

Kodi zingatheke bwanji kuti munthu asaone Njira yoperekedwa ndi Mulungu masiku ano? Koma ulemerero kwa Mulungu, ife tikhoza kuchiwona Icho, chifukwa ndife osankhidwa kuti tiziwone Izo. Ife sitinga, ndipo ife sitingakhoze kunyengedwa, chifukwa ife ndife Mawu Ake owonetseredwa.

Abale ndi alongo, lakani izi zilowetsedwa mphindi imodzi chabe, NDIFE MAWU AKUONETSEDWA!! Mulungu Mwiniwake, akuyankhula kupitira mu milomo ya munthu, akutiuza ife IFE NDIFE MAWU. Sitiyenera kuopa chilichonse. Zonse zomwe tikufuna ndi zathu.

Mlungu uliwonse timayembekezera kuti Yehova adzatichezera. Ife tiribe malo pano oti tikhazikike aliyense, ngakhalenso aliyense sangakhoze kubwera ku Jeffersonville, kodi ife timaba tumizira iwo Mawu kupitira mu njira ya intaneti.

Ife tiri mumanyumba zathu, mu mipingo yathu, m’magalimoto athu, tasonkhana mozungulira maikolofoni athu ku chokera dziko lonse, kuyembekezera Kubwela kwa Ambuye.

Iwo asonkhana pamodzi nafe ku Africa, kuyembekezera Kubwela kwa Ambuye. Iwo asonkhana pamodzi nafe ku Mexico, kuyembekezera Kubwela kwa Ambuye. Ku Ulaya, Scandinavia, Australia, Middle East, South America, kuchokera konse mu dziko lapansi, kuyembekezera Kubwela kwa Ambuye.

Ndipo ife tasonkhana kuno ku mpingo wakwathu, Kachisi, tikuyembekezera Kubwela kwa Ambuye. Ife tiri maningi ochuluka mu nthawi, koma ife tiri pamodzi monga chigawo chimodzi, okhulupirira, kumvetsera ku Liwu la Mulungu, kuyembekezera Kubwea kwa Mesiya.

Ndife anthu oyitanidwa ndi osankhidwa a Mulungu kuchokera mu m’badwo woyipa uno chifukwa cha Dzina Lake. Ife tikuyesedwa ndi kutsimikiziridwa kwa Satana kuti ndife Mawu. Ndife gawo la Mtengo wa Mkwati Wapachiyambi uwo. Ife tikuwona moyo wathu ukuwonetseredwa ndi Mawu amenewo.

Ndishosavuta kuti aliyense akhulupirire kuti Yesu anali yankho lachindunji ku ulosi uliwonse womwe uyenera kukwaniritsidwa mwa Iye, chifukwa akuyang’ana mmbuyo kuti awone zikuchitika. Koma mu m’badwo woipa wamakono uno, iwo akuchita chinthu chomwecho chimene iwo ankachichita apo, pochitanthauzira Icho mwanjira ina, ndipo awapangitsa anthu kupita mu zosokeretsa zamphamvu kuti akhulupirire bodza. Ngati iwo akanakhoza kokha kuzindikira Iwo ali Mawu omwewo a m’badwo uno akuwonetseredwa.

Pali chinthu chimodzi chokha chimene chingakhoze kubweretsa Mkwati pamodzi, Uthenga uwu. Pali chinthu chimodzi chokha chimene ife tonse tingagwirizane nacho, Uthenga uwu. Pali Liwu limodzi lokha limene latsimikiziridwa kuti liri KULANKULA AMBUYE, Liwu la Mulungu pa tepi.

Tsopano, mipingo yozizira basi, yofunda, yokhuthala, ndi zina zotero, za fioloje zopangidwa ndi anthu, zomwe sizikana; Osankhidwa sakanapereka tcheru kwa izo. Koma zili pamwamba apo pafupifupi ngati zenizeni. Kungosiya Mawu amodzi ndi zonse zomwe muyenera kuchita. Lonjezedwa za m’badwo; nthawi yabwino kwambiri! Akhristu, kulikonse, samalani ku nthawi limene tikukhalamo! Lembani pansi, ndi kuwerenga, ndi kumvetsera pafupi.

Mulungu wa m’badwo woipa uwu akuchita zonse zomwe angathe kuti anyenge anthu powasunga Mawu Ake otsimikiziridwa kwa iwo. Iye akuyesera kuti awapangitse iwo kusakhulupirira Mawu amodzi okha, monga iye anachitira kwa Eva pachiyambi.

Koma Mkwati wa Mawu wa Khristu akubwera ku Mutu. Timabwereranso kwa Mnzathu komwe tinayambira. Nthawi yotuluka yayandikira. Mulungu Abwela ku Mkwati Wake yemwe amakhala ndi Mawu Ake.

Mzimu Woyera uli pano ukuitana Mkwati wa Khristu. Iye akuchita izo mwa kutsimikizira Mawu Ake a lonjezo kwa Iye, a m’badwo uno, kusonyeza kuti Iwo ndi Khristu.

Palibe chachikulu kuchila kukhala olumikizana ndi Mkwati kuzungulira dziko, kumvetsera ku Liwu la Mulungu likuyankhula molunjika kwa inu. Palibe chifukwa choyembekezera, kudabwa kapena kupemphera zomwe mukumva ndi zoona. Pakuti Iwo ali OWLIKIRIKA YEKHA, KULANKULA MAWU YA AMBUYE.

Bwerani mudzatimvetsere:

Ndipo zitatha izi ndinaona mngelo wina akutsika Kumwamba, wakukhala nao mphamvu yaikuru; ndipo dziko lapansi linawalitsidwa ndi ulemerero wake.

Pa 12:00 P.M., nthawi ya Jeffersonville, monga ife tikumva: MULUNGU WANTHAWI YOIPA INO 65-0801M.

Bro. Joseph Branham

Malemba yo werenge pamene mukalibe kuvelera Uthenga:

Mateyu 24 mutu 27:15-23
Luka 17:30 St
Yohane 1:1/14:12
Machitidwe 10:47-48
1 Akorinto 4:1-5; chaputala 14
2 Akorinto 4:1-6
Agalatiya 1:1-4
Aefeso 2:1-2/4:30
2 Atesalonika 2:2-4 / 2:11
Ahebri mutu 7
1 Yohane chaputala 1 / 3:10 / 4:4-5
Chibvumbulutso 3:14/13:4/Mitu 6-8 ndi 11-12/18:1-5
Miyambo 3:5
Yesaya 14:12-14

23-0115 Iwo Odzozedwawo Pa Nthawi Yotsiriza

Uthenga: 65-0725M Iwo Odzozedwawo Pa Nthawi Yotsiriza

PDF

BranhamTabernacle.org

Okondedwa nkhosa Osonkhanina Mu khola,

Ndine wokhutitsidwa ndi woyamikira kwambiri kwa Ambuye kusonkhana ndi aliyense wa inu mu Khola la Nkhosa la Mulungu mlungu uliwonse, kumene timabisidwa mobisika, kudya ndi kukhala ndi Chakudya Chobisika chimenecho. Ndi Vumbulutso la Yesu Khristu, kudzitsimikizira ndi kudziulula Yekha kwa ife.

Iye wadzibisa Yekha kuti ena ayang’ana kumene pa Iwo ndipo sachiwona Iwo, koma kwa ife, Mkwati Wake wosankhidwa, ife tikuwona Iwo mwa mbalambanda ndi kukhulupirira Mawu aliwonse. Ife takhala ndi Mawu Ake ndi mneneri Wake monga iwo ali umodzi ndi umodzi.

Ndipo ngati inu muli mwana wa Mulungu, inu muzakhala ndi mneneri wa Baibulo ili. Ndi Mawu.

Aneneri ambiri odzozedwa masiku ano amati “Ndi Mzimu Woyera umene uyenera kukhala nawo, osati mneneri.” Monga aneneri akale, ngati ife tiri ndi funso, payenera kukhala yankho yamunshye. Ife tiyenera kuyenda KU MAWU kuti tikawone zomwe mneneri patsogolo pathu ananena.

Koma pali Mzimu wazohona wa Khristu, ndipo ndiwo Mawu osandulika thupi momwe analonjezera kuchita.

UMODZI weniweni wa Khristu Mzimu umene Iye analonjeza, Malaki 4, Luka 17, Mwana wa Munthu akudziulula Yekha mu thupi la munthu.

Inde, alipo amuna odzozedwa. Inde, ali nako kuitanidwa. Inde, iwo ali ndi Mzimu Woyera weniweni. Inde, ali ndi zolinga ndi zolinga zabwino.

Ndiye tingadziŵe bwanji chabwino ndi choipa?

Zindikirani, iwo akuwoneka chimodzimodzi. Iwo anadzozedwa chimodzimodzi. Koma zindikirani, “Ndi chipatso chawo…”

Ndimasonda kunena zinthu izi koma nthawi lachedwa ndipo nthawi ikuthawa. Izi ndi zimene zikunenedwa ndi kulalikidwa lero ndi mimbulu yolusa ija Paulo anachenjeza mpingo, ndi odzozedwa abodza M’bale Branham anati adzabwera. Iwo ali pano pakati pathu, monga ananenera.

Nayi gawo la kalata yolembedwa kuchokera kwa mtumiki. Chipatso chawo chikuyesa kukayikira mneneri wa Mulungu. Amachenjeza anthu awo kuti ife ndife opembedza potsatira Mneneri ndi Kutyanka Kuliza.

Mvetserani momwe izi ziliri zachinyengo.

Ndi makala wolakwilisidwa kuti chiwanda ichi chalowa muuthenga wathu kotero kuti tsopano timaitana afalitsa za maulaliki a William Branham kuti NDI MAWU A MULUNGU. William Branham sanali liwu lenileni la Mulungu, koma liwu la munthu amene Mulungu anamugwiritsa ntchito. Baibulo silimanena kuti iye anali liwu la Mulungu, koma Baibulo limamutchula iye monga liwu la mngelo wa 7. ( Chiv 3:14; 10:7 ).

Tiyeni tipite ku MAWU ndikulola mneneri wa Mulungu kuvumbulutsa chiphunzitso chonyenga ichi.

Ngati ndakulakwirani ndikunena zimenezo, ndikhululukireni, koma, ndinamva kuti mwina ndakhumudwa, koma, INE NDINE MAWU A MULUNGU KWA INU.

Tsopano kodi inu mukhulupirira ndani, mneneri wodzozedwa wabodza uyu, kapena MTUMIKI WA NGELO WACHISANU NDI CHIWIRI WA MULUNGU? Inu mungakhoze bwanji kukhala pansi pa mtumiki aliyense yemwe angakhulupirire kapena kukuphunzitsani inu zinthu izi? Inu chilibwino mulowe mu Mawu pamene nthawi ikaliko.

Kulakwitsa koyipa kwapangidwa ndi gulu la uthenga pomuyesa William Branham kukhala chishintilizo. William Branham sanali konse chishintilizo! Mawu a Mulungu ndiwo chishintilizo.

Amen, Mawu a Mulungu NDI chishintilizo chathu. Kodi Mawu anabwela kwa ndani, inu kapena IYE? Kodi wotanthauzira mwaumulungu wa MAWU A MULUNGU ndi ndani, inu kapena IYE? Ndi ndani yemwe Lawi la Moto linamutsimikizira kuti ali NDI MAWU AMBUYE, inu kapena IYE?

Chifukwa iwe umapeza amuna awiri, iwe uli nawo maganizo awiri.

Ife sitikufuna amuna awiri kapena maganizo awo, ife tifuna zomwe mneneri wa Mulungu ananena pa tepi.

Ndipo uyenera kufika ku chishintilizo chimodzi, ndipo chishintilizo changa ndi Mawu, Baibulo.

Ndi zimenezo, monga momwe munanenera, Baibulo ndi lake ndi chishintilizo lathu, koma kenako akuti:

Ndikudziwa kuti inu, abale athu, mumayang’ana kwa ine kuti ndine chishintilizo chanu.

Kotero yembekezani kamphindi, izo zikumveka zosiyana ndi zomwe MUNANENA. Iye anati ife timayang’ana kwa iye kukhala Chishintilizo chathu.

Molingana ngati ndimatsatira Mulungu, monga Paulo ananenera m’Malemba, “Inu munditsate ine, monga ine ndimatsatira Khristu.”

Kodi ameneyo si wodzozedwa? Kodi iye sankadziwa zimene ankanena?

Kodi mneneri wa Mulungu anatiuza chiyani sabata yatha?

Ife tikupeza kuti pamene munthu abwera, wotumizidwa kuchokera kwa Mulungu, wodzozedwa ndi Mulungu, ndi MAWU AMBUYE owona, uthenga ndi mthenga zimakhala mmodzi ndi mmodzi.

Anati simungawalekanitse, ali chinthu chimodzimodzi, koma inu mukuti tiyenera?

William Branham sali wosiyana ndi munthu aliyense wachivundi, pakuti iye anali munthu wa zikhumbo, monga analiri Eliya.

Ameni, iye anali munthu motsimikiza, koma iye anali MUNTHU amene Mulungu anamusankha kuti amuululireko Mawu Ake onse, ndi kutitsogolera ife ku Dziko Lolonjezedwa. Iye anali mmodzi yemwe Mulungu anati, apangitseni anthu kuti akukhulupirireni INU.

Chinthu chomwecho, odzozedwa, kulalikira Uthenga wa pentekoste, koma kukana lonjezo la tsiku-lino la Mawu kukhala likutsimikiziridwa, “Yesu Khristu yemweyo dzulo, lero, ndi nthawizonse.”

Kodi ife tingadziwe bwanji kusiyana kwake ngati iwo ali odzozedwa owona a Mzimu Woyera? Anatipatsa zitsanzo kuti tidziwe aneneri onyenga kuchokera kwa mneneri woona.

Balamu ndi Mose. Mikaya ndi Zedekiya. Yeremiya ndi
Hananiya. Muzochitika zonse onse awiri anali aneneri odzozedwa a Mulungu, koma kodi iye anatiuza kuti tichite chiyani, KHALANI NDI MNENERI WA MULUNGU WOYENZEKEZEKA. Imeneyi ndi njira YOKHALA yotsimikizira kuti mukutsatira Njira yoperekedwa ndi Mulungu, ndipo muli mu chifuniro Chake chanbwino.

Ine ndine mmodzi yekha amene ali pafupi pamene Iye azichita izo. Ine ndinali liwu lokha limene Iye ankagwiritsa ntchito, kuti azinene Izo. Sizinali zomwe ndimadziwa; ndi chimene ine ndinangodzipereka kwa icho ndekha, chimene Iye anachiyankhula nacho.

Ndizo zonse Mkwati akufuna ndi zosowa. Liwu Limodzi. Mneneri umodzi. Uthenga umodzi. Mtumiki umodzi.

O Atate, ndife othokoza bwanji chifukwa cha chisomo Chanu ndi chifundo kwa ife. Munatiuza kuti palibe chovuta ndi Inu. Palibe chovuta ndi ife. Pakuti zinthu zonse ndi zotheka kwa iwo amene akhulupirira, ndipo ife TIKHULUPIRIRA.

Bwerani mudzabwere nafe Lamlungu nthawi ya 12:00 P.M., nthawi ya Jeffersonville, pamene tili ndi Liwu losankhidwa ndi Mulungu limatiuza zonse za Odzozedwa Pa Nthawi Yotsiriza 65-0725M.

Bro. Joseph Branham

23-0108 Chakudya Chauzimu Mu Nyengo Yake

Uthenga: 65-0718E Chakudya Chauzimu Mu Nyengo Yake

PDF

BranhamTabernacle.org

Wokondedwa Wosakila

Pali chitsime cha Chivumbulutso chomwe chikutumphuka mkati mwathu kupambana kale lonse. Ife tamva Uthenga uwu moyo wathu wonse, ndipo nthawizonse takhala tikukhulupirira Mawu aliwonse, koma TSOPANO Iwo wakhala akuwonetseredwa mwa ife kupambana kale.

Tsopano ndi nthawi, tsopano ndi nyengo yomwe ife tikudyera pa zinthu zobisika za Mulungu zomwe zabisika kwa dziko. Chinthu chimene anthu amaseka ndi chinthu chimene timapempherera. Chinthu chimene anthu amaitana “kufunta,” timaitana “Chachikulu!” Mulungu watiululira kuti pali njira imodzi yokha yoperekedwa kunkala Mkwati Wake, KUTYANKA KULIZA.

Koma zikomo kwa Mulungu, tili ndi Chakudya chobisika, Chakudya chauzimu chomwe tikukhala pa ubwino ndi chifundo cha vumbulutso la Yesu Khristu m’masiku otsiriza ano, kudzitsimikizira ekha pakati pa anthu Ake.

Ndi Uthenga uliwonse umene Mkwati amamva, Amatsimikizira kwa ife kuti ndicho chifuniro Chake chabwino. Sizimene TIKUGANIZA kuti Iye akulankhula, komanso sizomwe TIKUGANIZA Izo zikutanthauza, NDI EXAKATILI zimene Iye Akunena ndipo ena sangathe kuziwona; iwo anavalika manso. Mulungu wazibisa Izo. Iwo amayang’ana kumene pa Iwo, koma samawawona Iwo. Kwa ife, NDI ZONSE TIZIONA.

Pamene tikusonkhana sabata iliyonse, sitingathe kunva zomwe Iye atiuze ndi kutiululira. Lamlungu lino, Iye satipatsa ife tinthu tating’ono tobisika, Atipatsa ife malo okhala ndi amayi ndi KULIBULA mobwerezabwereza kuti titsimikizire kuti tapeza.

Mneneri animals maningi mupulezensi ya Mulungu, aneneri a Chipangano Chakale, kapena nthawi iliyonse, pamene iwo amakhala mupulezensi ya Mulungu mpaka iwo akhala Mawu, Uthenga wawo ndi Mawu yameneo. Ndipo, kumbukirani, iye anati, “ KULANKULA KWA AMBUYE.”

Ife tikupeza kuti pamene munthu abwera, wotumizidwa kuchokera kwa Mulungu, wodzozedwa ndi Mulungu, ndi KULANKULA KWA AMBUYE , uthenga ndi mtumiki ali umodzi ndi umodzi.

Ndiye pamene munthu abwera ndi KULANKULA KWA AMBUYE, iye ndi Uthenga ali umodzi.

Kumwamba kumachikamba, Baibulo emachikamba, Uthenga umachikamba, chimodzimodzi.

Mneneri, Mawu, Uthenga; mutumiki, Uthenga, ndi Uthenga, zinali zimozimozi.

Munthu aliyense ndi uthenga wake ndi umodzi.

Kambiranani za Mgodi wa Golide.

Ngati muli ndi Chivumbulutso chilichonse, ndikuganiza kuti amamveketsa bwino; Uthenga ndi mtumiki ali CHIMODZI. Mukumva zomwe ananena…ZOMWEZI!! Ndiye inu simungakhoze kumulekanitsa mtumiki ku Uthenga, atumiki.

Muyenera kuyika MTUMIKI mu mpingo wanu pamodzi ndi UTHENGA umene anabweretsa kapena simukuvomereza UTHENGA WONSE. IWE SIULI MKWATI.

O! Apanso, zimapangitsa Uthenga ndi mutumiki kukhala amodzi. Chakudya chauzimu chakonzeka, ndipo Icho chiri mu nyengo tsopano.

Kwa ife, amene timakhulupirira ntawi ya Mulungu emene ife tikukhalamo, mtumiki yemwe Iye anamutumiza, Mawu aliwonse amene iye analankhula; zinthu izi ndi Chakudya chobisika.

Momwe ife tikukondera Uthenga uwu, ndipo pamene inu mukuganiza, “Pangakhale bwanji wochuluka?” Iye amaika mwala wapamutu pa Iwo potiuza ife yemwe ife tiri tsopano.

Kodi simukuwona ulamuliro wa Mulungu wamoyo mu Mpingo wamoyo, Mkwati? Odwala akuchiritsidwa, akufa aukitsidwa, olumala akuyenda, asaona akuwona, Uthenga ukupita mu mphamvu Yake, pakuti Uthenga ndi mtumiki ali yemweyo. Mawu ali mu Mpingo, mwa munthu.

Mawu amenewo MWA IFE. Ife ndife Uthenga. Ife tiri nawo ulamuliro. Uthenga uwu ndi ife NDI UMODZI!! Lankhulani za kubwebweta mobwerezabwereza.

Mkwati ndi gawo la Mwamuna, Mpingo ndi chimozimozi ndi Khristu. “Ntchito zimene Ine ndichita inunso mudzazichita.”

Ndife gawo la Mwamuna!!

NDIFE CHIMOZIMOZI NDI KHRISTU!!

Inu mukuganiza kuti zikumveka bwino tsopano, ndipo akudalitsa mtima Yanu mukuwerenga mawu awa, yembekezani mpaka inu mumve Liwu la Mulungu likukuwuzani izo kwa inu mulomo ndi khutu Lamlungu lino pa 12:00 p.M., nthawi ya Jeffersonville, pamene ife timva: 65-0718E. Chakudya Chauzimu Panyengo Yoyenera.

Mukuitanidwa kuti mubwere nafe. Ngati simungathe, TYANKANI KULIZA nthawi iliyonse, Uthenga uliwonse, kulikonse, ndipo imvani mtumiki wa Mulungu akukubweretserani Uthenga wa Mulungu.

Bro. Joseph Branham.

Kotero izo ziri lero, kuti Mkate wa Moyo umene ana amadyapo, umatsatira Uthenga wa Mulungu, kuti uwasamalire iwo mu nthawi ya chilala.

Malemba oti muwerenge
1 Mafumu 17:1-7 Amosi 3:7 Yoweli 2:28 Malaki 4:4 Luka 17:30 Yohane 14:12

22-1231 Mpikisano

Uthenga: 62-1231 Mpikisano

PDF

BranhamTabernacle.org

Wokondedwa Nkhosa Zam’dera,

Ndikufuna kudzakhalanso ndi Mgonero m’manyumba zathu pa Madzulo a Chaka Chatsopano, pa 31 December. Malangizo momwe mungapezere waini, ndi kuphika mkate wa Mgonero angapezeke m’malinki ali pansi. Linki yomunga daunilode wamawu amtunduwu upezeka posachedwa patsamba lathu. Kapena, munga lize mawu omvera kuchokera pa pulogalamu ya Lifeline.

Kwa anthu akudera la Jeffersonville, munga teng wainivi wa Mgonero pachisanu, Disembala 30, pakati pa 1:00 – 4:00 pm, pansi pa denga la VGR.

Timvera 62-1231 ku Shoshana, kuyambira 5:00 pm EST pa satade, Disembala 31st. M’bale Branham akadzabweretsa Uthenga wa Madzulo wa Chaka Chatsopano, tidzaimilika tepu ndikukhala ndi pafupifupi mphindi 10 za Nyimbo za Kulambira pamene tikukonzekera Mgonero wa Ambuye. tidzayamba anso tepi pamalo pomwe M’bale Branham ayambila utumiki wa Mgonero. Pa tepi iyi, iye wasiya kusambika mapazi gawo la utumiki, chimene ife tizachita.

Pamene tikutembenukira ku chaka china mu Utumiki Wake, tiyeni tiperekenso mwewo yathu kwa Iye mwatsopano kupitira mu kumva Mawu poyamba, ndiye kudya nawo Mgonero Wake. Ndi mwayi wamtengo wapatali bwanji umene tili nawo wokonza nyumba zathu kukhala Malo Opatulika kuti tilandire Mfumu ya Mafumu kuti ibwere kudzatigwirizanitsa ise.

Mulungu akudalitseni,

M’bale Joseph