22-1231 Mpikisano

Uthenga: 62-1231 Mpikisano

PDF

BranhamTabernacle.org

Wokondedwa Nkhosa Zam’dera,

Ndikufuna kudzakhalanso ndi Mgonero m’manyumba zathu pa Madzulo a Chaka Chatsopano, pa 31 December. Malangizo momwe mungapezere waini, ndi kuphika mkate wa Mgonero angapezeke m’malinki ali pansi. Linki yomunga daunilode wamawu amtunduwu upezeka posachedwa patsamba lathu. Kapena, munga lize mawu omvera kuchokera pa pulogalamu ya Lifeline.

Kwa anthu akudera la Jeffersonville, munga teng wainivi wa Mgonero pachisanu, Disembala 30, pakati pa 1:00 – 4:00 pm, pansi pa denga la VGR.

Timvera 62-1231 ku Shoshana, kuyambira 5:00 pm EST pa satade, Disembala 31st. M’bale Branham akadzabweretsa Uthenga wa Madzulo wa Chaka Chatsopano, tidzaimilika tepu ndikukhala ndi pafupifupi mphindi 10 za Nyimbo za Kulambira pamene tikukonzekera Mgonero wa Ambuye. tidzayamba anso tepi pamalo pomwe M’bale Branham ayambila utumiki wa Mgonero. Pa tepi iyi, iye wasiya kusambika mapazi gawo la utumiki, chimene ife tizachita.

Pamene tikutembenukira ku chaka china mu Utumiki Wake, tiyeni tiperekenso mwewo yathu kwa Iye mwatsopano kupitira mu kumva Mawu poyamba, ndiye kudya nawo Mgonero Wake. Ndi mwayi wamtengo wapatali bwanji umene tili nawo wokonza nyumba zathu kukhala Malo Opatulika kuti tilandire Mfumu ya Mafumu kuti ibwere kudzatigwirizanitsa ise.

Mulungu akudalitseni,

M’bale Joseph