23-0108 Chakudya Chauzimu Mu Nyengo Yake

Uthenga: 65-0718E Chakudya Chauzimu Mu Nyengo Yake

PDF

BranhamTabernacle.org

Wokondedwa Wosakila

Pali chitsime cha Chivumbulutso chomwe chikutumphuka mkati mwathu kupambana kale lonse. Ife tamva Uthenga uwu moyo wathu wonse, ndipo nthawizonse takhala tikukhulupirira Mawu aliwonse, koma TSOPANO Iwo wakhala akuwonetseredwa mwa ife kupambana kale.

Tsopano ndi nthawi, tsopano ndi nyengo yomwe ife tikudyera pa zinthu zobisika za Mulungu zomwe zabisika kwa dziko. Chinthu chimene anthu amaseka ndi chinthu chimene timapempherera. Chinthu chimene anthu amaitana “kufunta,” timaitana “Chachikulu!” Mulungu watiululira kuti pali njira imodzi yokha yoperekedwa kunkala Mkwati Wake, KUTYANKA KULIZA.

Koma zikomo kwa Mulungu, tili ndi Chakudya chobisika, Chakudya chauzimu chomwe tikukhala pa ubwino ndi chifundo cha vumbulutso la Yesu Khristu m’masiku otsiriza ano, kudzitsimikizira ekha pakati pa anthu Ake.

Ndi Uthenga uliwonse umene Mkwati amamva, Amatsimikizira kwa ife kuti ndicho chifuniro Chake chabwino. Sizimene TIKUGANIZA kuti Iye akulankhula, komanso sizomwe TIKUGANIZA Izo zikutanthauza, NDI EXAKATILI zimene Iye Akunena ndipo ena sangathe kuziwona; iwo anavalika manso. Mulungu wazibisa Izo. Iwo amayang’ana kumene pa Iwo, koma samawawona Iwo. Kwa ife, NDI ZONSE TIZIONA.

Pamene tikusonkhana sabata iliyonse, sitingathe kunva zomwe Iye atiuze ndi kutiululira. Lamlungu lino, Iye satipatsa ife tinthu tating’ono tobisika, Atipatsa ife malo okhala ndi amayi ndi KULIBULA mobwerezabwereza kuti titsimikizire kuti tapeza.

Mneneri animals maningi mupulezensi ya Mulungu, aneneri a Chipangano Chakale, kapena nthawi iliyonse, pamene iwo amakhala mupulezensi ya Mulungu mpaka iwo akhala Mawu, Uthenga wawo ndi Mawu yameneo. Ndipo, kumbukirani, iye anati, “ KULANKULA KWA AMBUYE.”

Ife tikupeza kuti pamene munthu abwera, wotumizidwa kuchokera kwa Mulungu, wodzozedwa ndi Mulungu, ndi KULANKULA KWA AMBUYE , uthenga ndi mtumiki ali umodzi ndi umodzi.

Ndiye pamene munthu abwera ndi KULANKULA KWA AMBUYE, iye ndi Uthenga ali umodzi.

Kumwamba kumachikamba, Baibulo emachikamba, Uthenga umachikamba, chimodzimodzi.

Mneneri, Mawu, Uthenga; mutumiki, Uthenga, ndi Uthenga, zinali zimozimozi.

Munthu aliyense ndi uthenga wake ndi umodzi.

Kambiranani za Mgodi wa Golide.

Ngati muli ndi Chivumbulutso chilichonse, ndikuganiza kuti amamveketsa bwino; Uthenga ndi mtumiki ali CHIMODZI. Mukumva zomwe ananena…ZOMWEZI!! Ndiye inu simungakhoze kumulekanitsa mtumiki ku Uthenga, atumiki.

Muyenera kuyika MTUMIKI mu mpingo wanu pamodzi ndi UTHENGA umene anabweretsa kapena simukuvomereza UTHENGA WONSE. IWE SIULI MKWATI.

O! Apanso, zimapangitsa Uthenga ndi mutumiki kukhala amodzi. Chakudya chauzimu chakonzeka, ndipo Icho chiri mu nyengo tsopano.

Kwa ife, amene timakhulupirira ntawi ya Mulungu emene ife tikukhalamo, mtumiki yemwe Iye anamutumiza, Mawu aliwonse amene iye analankhula; zinthu izi ndi Chakudya chobisika.

Momwe ife tikukondera Uthenga uwu, ndipo pamene inu mukuganiza, “Pangakhale bwanji wochuluka?” Iye amaika mwala wapamutu pa Iwo potiuza ife yemwe ife tiri tsopano.

Kodi simukuwona ulamuliro wa Mulungu wamoyo mu Mpingo wamoyo, Mkwati? Odwala akuchiritsidwa, akufa aukitsidwa, olumala akuyenda, asaona akuwona, Uthenga ukupita mu mphamvu Yake, pakuti Uthenga ndi mtumiki ali yemweyo. Mawu ali mu Mpingo, mwa munthu.

Mawu amenewo MWA IFE. Ife ndife Uthenga. Ife tiri nawo ulamuliro. Uthenga uwu ndi ife NDI UMODZI!! Lankhulani za kubwebweta mobwerezabwereza.

Mkwati ndi gawo la Mwamuna, Mpingo ndi chimozimozi ndi Khristu. “Ntchito zimene Ine ndichita inunso mudzazichita.”

Ndife gawo la Mwamuna!!

NDIFE CHIMOZIMOZI NDI KHRISTU!!

Inu mukuganiza kuti zikumveka bwino tsopano, ndipo akudalitsa mtima Yanu mukuwerenga mawu awa, yembekezani mpaka inu mumve Liwu la Mulungu likukuwuzani izo kwa inu mulomo ndi khutu Lamlungu lino pa 12:00 p.M., nthawi ya Jeffersonville, pamene ife timva: 65-0718E. Chakudya Chauzimu Panyengo Yoyenera.

Mukuitanidwa kuti mubwere nafe. Ngati simungathe, TYANKANI KULIZA nthawi iliyonse, Uthenga uliwonse, kulikonse, ndipo imvani mtumiki wa Mulungu akukubweretserani Uthenga wa Mulungu.

Bro. Joseph Branham.

Kotero izo ziri lero, kuti Mkate wa Moyo umene ana amadyapo, umatsatira Uthenga wa Mulungu, kuti uwasamalire iwo mu nthawi ya chilala.

Malemba oti muwerenge
1 Mafumu 17:1-7 Amosi 3:7 Yoweli 2:28 Malaki 4:4 Luka 17:30 Yohane 14:12