Ndandanda ya Khrisimasi

Okondedwa Abale ndi Alongo,

Chifukwa cha Khrisimasi ili pa mulugu chaka chino, ndamva mumtima mwanga kuti tisakhale ndi nthawi yoti timve Uthenga tsiku limenelo. Mabanja ambiri ali ndi ana ang’ono omwe amasangala kutsegula mphatso zawo m’mawa wa Khrisimasi, ndipo zingakhale zovuta kwa iwo kukhazikika kuti amve Uthenga kapena kuwapangitsa kuti ayembekeze mpaka nthawi ina.

Ndipo, komachabe, pa Khrisimasi, mukudziwa, ana aang’ono, sungawauze mosiyana. Iwo, basi, ndi nthawi ya Khrisimasi kwa iwo. Ndipo iwo siangankale apachikidwe masokosi awo aang’ono, pagankala chinachake. Ndi mwambo, ngakhale mu ziko lathu, kuti iwo amapachika sokosi, ndi chinachake chimzake. Bwanji, ine ndinatero, pamene ine ndinali mwana, ndipo—ndipo ngakhale monga—kutalika kwa Lemba, njira yopunthidwa monga iyo iliri. Koma, ana amamva ana ena akunena kuti, “Chabwino, ndalandira izi pa Khrisimasi. Ndapeza izi.” Ana aang’ono amaima pozungulira, langanani, inu mukudziwa. Inu, inu simungakhoze kuwapangitsa iwo kumvetsa. Mwaona? Chifukwa chake, Khrisimasi inabwela kunkala. Inde.

Pangakale ena omwe angakonde kuwuka kuseniseni ndikumva Uthenga, popeza ali ndi mapulani ndi achibale awo tsiku lomwelo. Choncho ndasankha kuti banja lililonse lisankhe nthawi yomwe ingagwirizane ndi nbanja yawo yomvera Uthenga. Tidzaulutsa Uthenga pa Lifeline katatu kosiyana pa Tsiku la Khrisimasi: 9:00 A.M. – 12:00 PM. – 5:00 P.M.. napapata musaganize kuti muyenera kumvelera imodzi mwa nthawizi, koma sankhani nthawi yabwino kwa inu kapena banja lanu. Chofunikira kwambiri ndichakuti, TYAKANI KULIZA.

Zingawoneke ngati zoseketsa, m’mawa uno, kuvala jasi langa papulatifomu, koma ndinali wokondwa—kusonyeza chikhoto chokongola chomwe chalitchi inandipatsa. Ine ndinamuwona M’bale Neville kuno tsiku lina, anavala suti yabwino iyo, momwe iyo inamukwanira iye koma kwambiri, ndipo ine ndinaganiza, chabwino, ine—ine…izo zinawoneka zabwino kwambiri, ndipo osonkhana akulankhula za izo, ine ninaganiza, “Ine Ndingovala chijasi changa papulatifomu.” Ine basi…

Mukudziwa, ndikulupirira kuti sitikula. Nthawi zonse…Ndipo sindikufuna kukula. Nanga bwanji izo, M’bale Luther? Ayi, sindikufuna kukula. Timafuna kukhalaxhabe ana nthawi zonse.

Ambuye akupatseni inu olide lodabwitsa lodzaza ndi Kukhalapo Kwake.

Bro. Joseph Branham